05/01/2025
Ndipo musakayike imfa ik*tidikila ,manda ak*tidikilaso ,angele amafuso akudikilaso ,mphusi zik*tidikla ,zosezitu apa ndimasauso owonekela ,,udandaulileni Moyo wanu ndipo ziganizileni k*t kod zikandithala bwanji manda ,ndipo Allah akulakhula mu Qur'an
وَجَاءَتْ سَكْرَةُ الْمَوْتِ بِالْحَقِّ ۖ ذَٰلِكَ مَا كُنتَ مِنْهُ تَحِيدُ Ndipo kuledzera kwa imfa kukam'dzera Mwa choona, (pamenepo adzauzidwa): 'Ichi ndi chomwe mumachithawa chija.',,,,,,
Ndithudi ili ndsku lamasauso kwa anthu osasamala swalah ndizintchto zina zabwino ,,,,,,,,,
Ndipo musaone ngat Allah sali nanu pafupi ,,gwilani ntchito iliyoseyo ndipo Angelo akulemba choipa(or zolakhula zanu samalani) ,or chabwino ndipo sapanga mistake
مَّا يَلْفِظُ مِن قَوْلٍ إِلَّا لَدَيْهِ رَقِيبٌ عَتِيدٌ
Palibe chilichonse chimene Amayankhula koma pafupi ndi iye pali Mlonda amene wakonzekera (kulemba).